Here in mangochi kwa Makawa the roads are very bad so we need help, we once talked to our councillor but no help.
Nseu wa ku ma puloti suli bwino kukagwa mvula timavutika chifukwa cha matope ma galimoto amavutika kuyenda, nazo njinga sitimayendesa chifuka cha ku telela kwa mu nseu....tinawauza a MP anthu koma anangobweletsa nchenga komano ntchito siyinayambike
kuno kwathu ku chingale Zomba mlatho unakokoloka a MP anthu sitinawauze chifukwa amafika kuno nthawi ya campaign ... pano amakhala ku town tilibe angatithandize
kuno Kwathu ku Dedza pa Chimbiya kulibe nseu wolongosoka kupita ku St Kizito tinawafotokozela a MP anthu ndipo anati atithandiza ndee maso anthu ali ku njira kuyang'anira kwa MP
Kuno kwathu miseu silibwino. tufuna langizo kuti tingasate bwino m'mene ndalama zokonzera mseu zidagwirira ntchito
Would like to thank the Lilongwe City Council for upgrading the Area 36 Road. This is what we call development
Zolozolo East tupempha Khansala withu kuti watinozgere bridge kwa juma
in our ward through masaf 4 program we are opening two new roads one is from tongole to chadza and other from mchitanjiru to chikungu. and also through cdf we are constructing bridge at chadza to chiwoko river. Councilor Sese ward
BRIDGE KU ZOLOZOLO EAST MUGANTHILA LASUZGA. NYENGO YA MVULA WATHU WANGAJUMPHA YAYE WANOZGERETU
kuno ku Lupaso mseu uwo wufika pa Dec uli makora yaye, unozgeke sono chifukwa na mvula pazamusugza
Kuno ku Namiyango bwana MP Atikonzere nseu from Tondole to Weaving Factory