Our MP should lobby for the support of MRCS to construct toilets at Kaufulu primary as they have done in other primary schools through their WASH project. I feel sorry when am passing through the school and see the toilets that they use. It has to be understood that a good learning environment is essential
Kuno ku Zolozolo East tikulira chifukwa cha kukwera kwa school fund kufuma pa K1700 kufika pa K3000. mphakusugza kuti wanyakhe wakwaniske kweni Boma likuti likukhumba mwana waliyose walute ku school
School yakwathu ilibe ma desk since 1994 anatichotsera centre yamayeso chifukwa choti palibe madesk. Mbazi L E A primary school Dedza northwest constituency.
Ndati ndikambepo kuti tidapempha kudzera mwa atsogoleri athu pa kanthawi ndipo tidakali kudikilira kuti achitepo kanthu pa mavuto omwe ali pa sukulu ya Makata primary. ma toilet ogwira ntchito alipo atatu okha koma pali ma sauzande chiwerengero cha ana omwenso aziphunzitsi awo ndi ochepa. ine Kenson Malango kwa Chinseu.
School yakwathu ilibe ma desk since 1994 anatichotsera centre yamayeso chifukwa choti palibe madesk.
Khansala wathu kuno ku Tsabango 2 akuchita bwino mogwirizana ndi bungwe la Action Aid kuti ana adzipita kusukulu
akhansala kapena MP adera lathu, tithandizeni(ife Aphunzitsi ndi ophunzira pa Lizulu Primary school) potikozera Mzamani ground.Mr M.I Shaba.Lizulu,Ntcheu.
mutiunikilepo kuti kasi ntchakwenerera kuwezga mwana wa school kuti wakatole ndalama ya chitukuko , mayeso apo wanyake wakulemba mayeso? Kuno ku zolozolo tiphulani mu suzgo ili of which tindafike pa conclusion kuti tipereke ma 3000 poti apo wakachemeska tawapapi tikakana amount iyi kweni wasambizi wawezga wana cos of this money of which boma likukana kuti primary level njaulele except ndalama yamayeso
Let me commend Heart to Heart foundation for their initiative of giving out sanitary facilities in primary schools. I believe if a number of organisations can strive to support the government with such initiatives, education will prosper
Ine monga m'modzi mwa kholo lomwe lili ndi mwana wa sukulu pa Nkolokoti ndati ndiyamikire khama la aziphunzitsi apa sukuluyi
Ine ndati ndiwafikire nawo uthenga woyamba olemekezeka bambo Litchowa omwe apambana pa ukhansala kuno ku Ndirande Makata. Tikudziwa ntchito si yawo yokha ndipo akuyenera kugwira limodzi ndi Phungu ndinso kukhonsolo koma alingalire izi: 1. Pa sukulu ya Makata ma toilet okwanira palibe 2. Pa msika wa Makata pakufunika chi bin chotayilamo zinyalala. 3. Miseu yomwe idalowa mkati yambiri silibwino. Atipemphereko kuti azapale monga adapangira ku madera ena ngati Bangwe
Ku nkhani ya maphunziro kuno kwa chiuzira ku Lilongwe, dandaulo lathu ndilakuti pa school pali ana ambiri pamene ma block ndi ochepa zomwe zimapangitsa kukhala ana oposa 100 mu class imodzi zomwe zingapangitse kupatsirana matenda odzera mu mpweya komanso kovuta kwa ena kuti aphunzire bwino