m'mene unangopangika msonkhano kuno ku Ndilande wozamisa demokalase kudela lathu pano anthu otolela ndalama pa mwamba pa yomwe timapereka kale ya market fees anasiya.tikukhulupirira kuti izi ndi chifukwa cha msonkhano wa tilitonse pomwe tidapasidwa mwayi wofunsa aChairman amu nsika ndi a-Khonsolo ya mzinda wa Blantyre kuti afotokoze bwino kuti ndalama imeneyi imapita kuti chifukwa chitukuko sitimachiona.
As it can be observed in the attached picture, waste has accumulated dangerously in Falls close to Msonkhamanja CCAP. This is because over the past two weeks the City Council did not come through to empty the waste storage dustbin at the dumping site. This is not only an eye sore but also a health threat. Action should be taken and fast.
Let me commend Heart to Heart foundation for their initiative of giving out sanitary facilities in primary schools. I believe if a number of organisations can strive to support the government with such initiatives, education will prosper
I would like to comment on an article that was carried in The Nation newspaper about CSO's raising a concern on the decline in the Health Sector budget allocation over the last 5 years... it is worrisome when we are assured that it is okay and yet within the same week we heard that QECH is running short of theatre equipment
We would like to inform all our valued customers that our water production is still below the required capacity. This has resulted in some areas having low or no water supply for prolonged periods. To ensure equitable supply of water, we are therefore continuing with the Rationing Program. Please be assured that normal water supply in all the areas will resume as soon as the situation improves. We really regret for any inconvenience that this may cause. Attached is the Water Rationing Schedule starting from Saturday 24th December, 2016 to Friday 30th December, 2016. MANAGEMENT
Tiyamikire kuno ku Area 25 lero mmene kwachera magetsi sadazimeko. Bright Chagoma - Youth with a vision
Kuno kwa gwaza Chipatala Anachiyamba 2004 mpaka 2016 Palibe Chilipo Zomba Chingale. Ine Mayikolo
Ine ndim'nyamata ochokela ku chiladzulu south,koma khawa zanga zili pa khansala wanthu naphiyo,pali mulatho wachimwawa umene walumikiza mafumu awili,asakwata komaso mangulama mulatho wapakati pamafumu awili amenewa sulibwino konse,moti sindikudziwa ngati phungu wadela limeneli amene ali josefe mwanamvekha akudziwa zamavuto amenewa,mwachidule inu a Mzinda tapitani kuchiladzulu south kwa t/a nkalo mudzi mwamatope,siliya,ngoniwa,misomali,sakwata,mangulama,mwamidzi yochepa chabe muone mabvuto,ndimakuvetsesani ndim'mene mumapangila kapena kufufuzila zinthu, ine dzinalanga ndi evans mpethela namuku
I am Mike Kasiyafumbi from Area 23 Benito. I would like to know why ESCOM is taking long to come and fix poles when the Transformer was planted some time back.
ndati ndithirepo ndemanga pa nkhani ya achinyamata yomwe mumakambirana mu puloglamu ya pa radio lero. Palibe munthu wachikulire amene angakane kugwira ntchito ndi achinyamata, pokhapokha ngati pali chokaikitsa pa machitidwe ndi khalidwe la anyamatawo. Achinyamata tili nawo m'makwalalamu, kuchulukana ULESI. Ambiri akangophunzira pang'ono angofuna kufikira pa mpando olamulira, oyang'anira osafuna kugwira dotting. Kudzitukumula pakati pa akulu. Iai, dziwani kuti ngakhale adindo, atsogoleri a lerowa sanangofikira pamenepo. Nawonso Analinso achinyamata. Tatiyeni tidekhe, tiphunzire kuti tidzakhale adindo odalilika. You want to come from the classroom, straight into the State House! No, let us have time to learn the works in order to gain experience. I am Gogo Phiri in A49.
I am Victor Dzimbiri from Kawale 2. I would like to comment on today's Mzinda radio program about the participation of the youth in development. I wish to say that here in Kawale there is a youth centre near Masintha hall but there is no initiative from our leaders or organisations to make it work. if they can take the initiative to involve us we are ready to utilise it
Kuno ku lilongwe city west timangomva mmadera azathu chitukuko kunoko kwa mtsiliza ndimavuto chonde tingapite kuti kuti adundo athu atifike moti sitiwadziwa. Ine okhudzidwa ndi dera langa Harold phili
Ife kuno ku Area 23(Mtambalale,Zion,Ku zikiti,Tnm Transmiter & KK stores) timakhala opanda madzi nthawi yayitali chifukwa chiani?mwina pa mwezi kamodzi.Pliz help us.Kelvin Munthali-Mtambalale.
kuno ku Chiladzulu T.A.Kadewele chipatala chinayamba kumangidwa 2O14 mpaka lelo sichikutha
Kuchokera ku Chiwembe tikudandaula, Pipe ya sewage inathoka kalekale moti nyasi zikukolezera matendakwa anthu kuno ndinso opanga biziness mu nsika wa limbe
Why is lilongwe water board not installing pre paid meters.